Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 23:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo Alevi ndi Ayuda onse anacita monga mwa zonse anawauza Yehoyada wansembe; natenga yense amuna ace alowe dzuwa la Sabata pamodzi ndi oturuka dzuwa la Sabata; pakuti Yehoyada wansembe sanamasula zigawo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 23

Onani 2 Mbiri 23:8 nkhani