Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 21:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atate wao anawapatsa mphatso zazikuru, za siliva, ndi za golidi, ndi za mtengo wace, pamodzi ndi midzi yamalinga m'Yuda; koma ufumu anauninkha kwa Yehoramu; pakuti ndiye mwana wace woyamba.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 21

Onani 2 Mbiri 21:3 nkhani