Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Solomo anatumiza kwa Huramu mfumu ya Turo, ndi kuti, Monga momwe munacitira Davide atate wanga, ndi kumtumizira mikungudza yommangira nyumba yokhalamo, mundicitire ine momwemo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 2

Onani 2 Mbiri 2:3 nkhani