Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 16:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi cimodzi ca Asa, Basa mfumu ya Israyeli anakwera kulimbana ndi Yuda, namangitsa Rama, kuwaletsa anthu asaturuke kapena kulowa kwa Asa mfumu ya Yuda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 16

Onani 2 Mbiri 16:1 nkhani