Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 14:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi Asa ndi anthu anali naye anawalondola mpaka ku Gerari, nagwa Akusi ambiri osalimbikanso mphamvu iwowa; pakuti anathyoledwa pamaso pa Yehova ndi ankhondo ace; ndipo anatenga zofunkha zambiri.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 14

Onani 2 Mbiri 14:13 nkhani