Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 13:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo amuna a Yuda anapfuula cokweza; ndipo popfuula amuna a Yuda, kunacitika kuti Mulungu anakantha Yerobiamu ndi Aisrayeli onse pamaso pa Abiya ndi Yuda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:15 nkhani