Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 13:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo taonani, Mulungu ali nafe, wotitsogolera ndi ansembe ace, ndi malipenga oliza nao cokweza, kukulizirani inu cokweza. Ana a Israyeli inu, musalimbane naye Yehova Mulungu wa makolo anu; pakuti simudzapindula nako.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:12 nkhani