Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 13:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nafukizira Yehova nsembe zopsereza m'mawa ndi m'mawa, ndi madzulo onse, ndi zonunkhira za pfungo lokoma, nakonza mkate woonekera pa gome lopatulika, ndi coikapo nyali cagolidi ndi nyali zace, ziyake madzulo onse; pakuti tisunga cilangizo ca Yehova Mulungu wathu, koma inu mwamsiya Iye.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:11 nkhani