Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 11:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo analimbikitsa ufumu wa Yuda, nalimbikitsa Rehabiamu, mwana wa Solomo zaka zitatu; pakuti anayenda m'njira ya Davide ndi Solomo zaka zitatu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 11

Onani 2 Mbiri 11:17 nkhani