Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 10:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, popeza atate wanga anakusenzetsani goli lolemera, ine ndidzaonjezerapo pa goli lanu; atate wanga anakukwapulani ndi zikoti, koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 10

Onani 2 Mbiri 10:11 nkhani