Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 6:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atalawirira mamawa mnyamata wa munthu wa Mulungu, naturuka, taonani, khamu la nkhondo linazinga mudzi ndi akavalo ndi magareta. Ndi mnyamata wace ananena naye, Kalanga ine, mbuye wanga! ticitenji?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:15 nkhani