Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 6:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mtima wa mfumu ya Aramu unabvutika kwambiri pa icico, naitana anyamata ace, nanena nao, Kodi simudzandiuza wina wa ife wobvomerezana ndi mfumu ya Israyeli ndani?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:11 nkhani