Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 6:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu ya Israyeli inatumiza kumene munthu wa Mulungu anamuuzako ndi kumcenjeza; nadzisunga osapitako, kawiri kawiri.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:10 nkhani