Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 5:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova akhululukire mnyamata wanu mwa ici; akalowa mbuye wanga m'nyumba ya Rimoni kulambiramo, nakatsamira pa dzanja langa, nanenso ndikagwadira m'nyumba ya Rimoni, pakugwadira ine m'nyumba ya Rimoni, Yehova akhululukire mnyamata wanu mwa ici.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 5

Onani 2 Mafumu 5:18 nkhani