Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 5:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elisa anamtumira mthenga, ndi kuti, Kasambe m'Yordano kasanu ndi kawiri, ndi mnofu wako udzabwerera momwe, nudzakhala wokonzeka.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 5

Onani 2 Mafumu 5:10 nkhani