Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 3:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anagwira mwana wace wamwamuna woyamba amene akadakhala mfumu m'malo mwace, nampereka nsembe yopsereza palinga. Ndipo anakwiyira Israyeli kwambiri; potero anamcokera, nabwerera ku dziko lao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 3

Onani 2 Mafumu 3:27 nkhani