Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 3:26-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ndipo ataona mfumu ya Moabu kuti nkhondo idamlaka, anapita nao anthu mazana asanu ndi awiri akusolola lupanga, kupyola kufikira kwa mfumu ya Edomu, koma sanakhoza.

27. Pamenepo anagwira mwana wace wamwamuna woyamba amene akadakhala mfumu m'malo mwace, nampereka nsembe yopsereza palinga. Ndipo anakwiyira Israyeli kwambiri; potero anamcokera, nabwerera ku dziko lao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 3