Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 3:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti atero Yehova, Simudzaona mphepo, kapena kuona mvula, koma cigwaco cidzadzala ndi madzi; ndipo mudzamwa inu, ndi ng'ombe zanu, ndi zoweta zanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 3

Onani 2 Mafumu 3:17 nkhani