Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 25:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma kunena za anthu otsalira m'dziko la Yuda, amene adawasiya Nebukadinezara mfumu ya Babulo, iyeyu anamuika Gedaliya mwana wa Ahikamu mwana wa Safani akhale wowalamulira.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 25

Onani 2 Mafumu 25:22 nkhani