Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 20:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yesaya mneneri anadza kwa mfumu Hezekiya, nati kwa iye, Anatani anthu awa? anadza kwa inu kufumira kuti? Nati Hezekiya, Afumira dziko la kutari ku Babulo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 20

Onani 2 Mafumu 20:14 nkhani