Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 20:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hezekiya anawamvera, nawaonetsa nyumba yonse ya cuma cace, siliva, ndi golidi, ndi zonunkhira, ndi mafuta okometsetsa, ndi nyumba ya zida zace, ndi zonse zopezeka pacuma pace; panalibe kanthu m'nyumba mwace, kapena m'ufumu wace wonse osawaonetsa Hezekiya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 20

Onani 2 Mafumu 20:13 nkhani