Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 13:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkwiyo wa Yehova unayaka pa Israyeli, nawapereka m'dzanja la Hazaeli mfumu ya Aramu, ndi m'dzanja la Benihadadi mwana wa Hazaeli, masiku onsewoo

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 13

Onani 2 Mafumu 13:3 nkhani