Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 13:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elisa anadwala nthenda ija adafa nayo, namtsikira Yoasi mfumu ya Israyeli, namlirira, nati, Atate wanga, atate wanga, gareta wa Israyeli ndi apakavalo ace!

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 13

Onani 2 Mafumu 13:14 nkhani