Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 12:15-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Ndipo sanawerengera anthu, amene anapereka ndaramazi m'manja mwao kuti apatse ogwira nchito; popeza anacita mokhulupirika.

16. Ndarama za nsembe zoparamula ndi ndarama za nsembe yaucimo sanabwera nazo ku nyumba ya Yehova; nza ansembe izi.

17. Pamenepo Hazaeli mfumu ya Aramu anakwera, nathira nkhondo pa Gati, naulanda, nalunjikitsa nkhope yace kukwera ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 12