Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 12:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yoasi mfumu ya Yuda: anatenga zopatulika zonse adazipatula Yehosafati, ndi Yoramu, ndi Ahaziya, makolo ace, mafumu a Yuda, ndi zopatulika zace zace, ndi golidi yense anampeza pa cuma ca nyumba ya Yehova, ndi ca nyumba ya mfumu, nazitumiza kwa Hazaeli mfumu ya Aramu; motero anabwerera kucoka ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 12

Onani 2 Mafumu 12:18 nkhani