Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 10:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, powafika kalatayo, anatenga ana a mfumu, nawapha amuna makumi asanu ndi awiri, naika mitu yao m'mitanga, naitumiza kwa iye ku Yezreeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:7 nkhani