Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 10:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nalowa Yehu ndi Yehonadabu mwana wa Rekabu m'nyumba ya Baala, nati kwa otumikira Baala, Mufunefune, nimuone asakhale nanu muno otumikira Yehova, koma otumikira Baala okha.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:23 nkhani