Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kale m'Israyeli, munthu akati afunse kwa Mulungu, adafotero kuti, Tiyeni tipite kwa mlauliyo; popeza iye wochedwa mneneri makono ano, anachedwa mlauli kale.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9

Onani 1 Samueli 9:9 nkhani