Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 9:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali munthu Mbenlamlni, dzina lace ndiye Kisi, mwana wa Abiyeli, mwana wa Zerori, mwana wa Bekorati, mwana wa Afiya, mwana wa Mbenjamini, ndiye ngwazi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9

Onani 1 Samueli 9:1 nkhani