Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 6:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo amenewa ndiwo mafundo agolidi amene anabwezera kwa Yehova akhale nsembe yoparamula, kwa Asidodi limodzi, kwa Gaza limodzi, kwa Asikeloni limodzi, kwa Gati limodzi, kwa Ekroni limodzi;

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 6

Onani 1 Samueli 6:17 nkhani