Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 4:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene anthu anafika ku zithandozo, akuru a Israyeli anati, Yehova anatikanthiranji lero pamaso pa Afilisti? Tikadzitengere likasa la cipangano la Yehova ku Silo, kuti likabwera pakati pa ife, lidzatipulumutsa m'dzanja la adani athu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 4

Onani 1 Samueli 4:3 nkhani