Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 4:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo munthu wa pfuko la Benjamini anathamanga kucokera ku khamu la ankhondo, nafika ku Silo tsiku lomwelo, ndi zobvala zace zong'ambika, ndi dothi pamutu pace.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 4

Onani 1 Samueli 4:12 nkhani