Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 31:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Afilisti anaponyana ndi Aisrayeli; Aisrayeli nathawa pamaso pa Afilisti, nagwa olasidwa m'phiri la Giliboa.

2. Ndipo Afilisti anapitikitsa, osawaleka Sauli ndi ana ace; ndipo Afilisti anapha Jonatani, ndi Abinadabu, ndi Malikisua, ana a Sauli.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 31