Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 30:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anafunsira kwa Yehova, nati, Ndikalondola khamulo ndidzalipeza kodi? Ndipo anamyankha kuti, Lonriola, pakuti zoonadi udzawapeza, ndi kulanditsa zonse.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30

Onani 1 Samueli 30:8 nkhani