Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 28:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkaziyo anafika kwa Sauli, naona kuti ali wobvutika kwambiri, nanena naye, Onani, mdzakazi wanu anamvera mau anu, ndipo ndinataya moyo wanga, ndi kumvera mau anu munalankhula ndi ine.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28

Onani 1 Samueli 28:21 nkhani