Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 28:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anati kwa Akisi, Potero mudzadziwe cimene mnyamata wanu adzacita. Ndipo Akisi anati kwa Davide, Cifukwa cace ndidzakuika iwe ukhale wondisungira moyo wanga masiku onse.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 28

Onani 1 Samueli 28:2 nkhani