Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 26:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Sauli namanga zithando m'phiri la Hagila kupenya kucipululu kunjira, Koma Davide anakhala kucipululu, naona kuti Sauli alikumfuna kucipululu komweko.

4. Cifukwa cace Davide anatumiza ozonda, nazindikira kuti Sauli anabwera ndithu,

5. Ndipo Davide ananyamuka nafika pamalo pala Sauli anamangapo; ndipo Davide adaona pogona Sauli, ndi Abineri mwana wa Neri kazembe wa khamu lace; ndipo Sauli anagona pakati pa linga la magareta, ndipo anthu adamanga zithando pomzinga pace.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 26