Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 26:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ici unacicita siciri cabwino. Pali Yehova, muyenera kufa inu, cifukwa simunadikira mbuye wanu, wodzozedwa wa Yehova. Ndipo tsono, penyani mkondo wa mfumu ndi cikho ca madzi zinali kumutu kwace ziri kuti?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 26

Onani 1 Samueli 26:16 nkhani