Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 25:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Samueli anamwalira; ndi Aisrayeli onse anaunjikana pamodzi nalira maliro ace, namuika m'nyumba yace ku Rama. Davide nanyamuka, natsikira ku cipululu ca Parana.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:1 nkhani