Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 24:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Bwino lace Davide yemwe ananyamuka, naturuka m'phangamo, napfuulira Sauli, nati, Mbuye wanga, mfumu. Ndipo pakuceuka Sauli, Davide anaweramira nkhope yace pansi, namgwadira.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 24

Onani 1 Samueli 24:8 nkhani