Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 24:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pakutsiriza Davide kulankhula mau awa kwa Sauli, Sauli anati, Ndiwo mau ako kodi, mwana wanga Davide? Sauli nakweza mau ace, nalira misozi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 24

Onani 1 Samueli 24:16 nkhani