Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 24:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Onani, lero lomwe maso anu anapenya kuti Yehova anakuperekani inu lero m'dzanja langa m'phangamo, ndipo ena anandiuza ndikupheni; koma ndinakulekani, ndi kuti, Sindidzatukulira mbuye wanga dzanja langa; cifukwa iye ndiye wodzozedwa wa Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 24

Onani 1 Samueli 24:10 nkhani