Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 22:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kuti inu nonse munapangana dwembu pa ine, ndipo palibe wina wakundiululira kuti mwana wanga anapangana pangano ndi mwana wa Jese, ndipo palibe wilia wa inu wakundidtira cifundo kapena kundidziwitsa kuti mwana wanga anafulumiza mnyamata wanga kundilalira monga lero lomwe?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 22

Onani 1 Samueli 22:8 nkhani