Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 22:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Ahimeleki anayankha mfumu, nati, Ndipo ndani mwa anyamata anu onse ali wokhulupirika ngati Davide amene, mkamwini wa mfumu; wakuyenda mu uphungu wanu, nalemekezeka m'nyumba mwanu?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 22

Onani 1 Samueli 22:14 nkhani