Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 2:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzali kuti yense wakusiyidwa wa m'banja lako adzabwera kwa iye nadzawerama ndi kupempha ndalama ndi cakudya, nadzati, Mundipatsetu nchito yina ya wansembe, kuti ndikaona kakudya.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 2

Onani 1 Samueli 2:36 nkhani