Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 2:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Eli anadalitsa Elikana ndi mkazi wace, nati, Yehova akupatse mbeu ndi mkazi uyu m'malo mwa iye amene munampempha kwa Yehova. Ndipo iwowa anabwera kwao.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 2

Onani 1 Samueli 2:20 nkhani