Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:52 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu a Israyeli ndi Ayuda ananyamuka, napfuula, nathamangira Afilistiwo, mpaka ufika kucigwako, ndi ku zipata za Ekroni. Ndipo Afilistiwo olasidwa anagwa pa njira ya ku Saraimu, kufikira ku Gad ndi ku Ekroni.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:52 nkhani