Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:51 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Potero Davide anathamanga naima pa Mfilistiyo, nagwira lupanga lace, nalisolola m'cimace, namtsiriza nadula nalo mutu wace. Ndipo pakuona Afilisti kuti ciwinda cao cidafa, anathawa.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:51 nkhani