Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:49 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anapisa dzanja lace m'thumba mwace, naturutsamo mwala, nauponya, nalasa Mfilistiyo pamphumi; ndi mwalawo unalowa m'mphumi, ndipo iye anagwa pansi cafufumimba.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:49 nkhani