Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Davide, Yehova wakundipulumutsa pa mphamvu ya mkango, ndi mphamvu ya cimbalangondo, Iyeyu adzandipulumutsa m'dzanja la Mfilisti uyu, Ndipo Sauli anati kwa Davide, Muka, Yehova akhale nawe.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:37 nkhani